Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • nwt tsamba 2234-2235
  • B12-A Wiki Yomaliza ya Moyo wa Yesu Padziko Lapansi (Gawo 1)

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • B12-A Wiki Yomaliza ya Moyo wa Yesu Padziko Lapansi (Gawo 1)
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Yerusalemu ndi Madera Ozungulira
  • Nisani 8 (Sabata)
  • Nisani 9
  • Nisani 10
  • Nisani 11
  • B12-B Wiki Yomaliza ya Moyo wa Yesu Padziko Lapansi (Gawo 2)
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Ndandanda Yowerengera Baibulo pa Nyengo ya Chikumbutso cha 2023
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Ndandanda Yowerengera Baibulo pa Nyengo ya Chikumbutso cha 2022
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Ndandanda Yowerengera Baibulo pa Nyengo ya Chikumbutso cha 2024
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2024
Onani Zambiri
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
B12-A Wiki Yomaliza ya Moyo wa Yesu Padziko Lapansi (Gawo 1)

B12-A

Wiki Yomaliza ya Moyo wa Yesu Padziko Lapansi (Gawo 1)

Losindikizidwa
Tchati chosonyeza zimene zinachitika mu 33 C.E., chaka chimene Yesu anaphedwa.

Yerusalemu ndi Madera Ozungulira

Mapu a Yerusalemu ndi madera ozungulira. Mapuwa akusonyeza madera odziwika komanso amene akuwaganizira. 1. Kachisi. 2. Munda wa Getsemane. 3. Nyumba ya Bwanamkubwa. 4. Nyumba ya Kayafa. 5. Nyumba imene Herode Antipa ankakhala. 6. Damu la Betizata. 7. Dziwe la Siloamu. 8. Holo ya Khoti Lalikulu la Ayuda. 9. Gologota. 10. Munda Wamagazi.
  1. Kachisi

  2. Munda wa Getsemane (?)

  3. Nyumba ya Bwanamkubwa

  4. Nyumba ya Kayafa (?)

  5. Nyumba imene Herode Antipa ankakhala (?)

  6. Damu la Betizata

  7. Dziwe la Siloamu

  8. Holo ya Khoti Lalikulu la Ayuda (?)

  9. Gologota (?)

  10. Munda Wamagazi (?)

Sankhani tsiku: Nisani 8 | Nisani 9 | Nisani 10 | Nisani 11

Nisani 8 (Sabata)

MADZULO (Masiku a Ayuda amayamba ndi kutha dzuwa litalowa)

  • Anafika ku Betaniya kutatsala masiku 6 kuti Pasika achitike

  • Yohane 11:55–12:1

M’MAWA

MADZULO

Bwererani koyambirira

Nisani 9

MADZULO

  • Anakadya kunyumba ya Simoni wakhate

  • Mariya anadzoza Yesu mafuta a nado

  • Ayuda anabwera kudzaona Yesu ndi Lazaro

  • Mateyu 26:6-13

  • Maliko 14:3-9

  • Yohane 12:2-11

M’MAWA

  • Yesu wakwera bulu wamng’ono ndipo gulu la anthu amene akusangalala akuyala zovala komanso nthambi za kanjedza mumsewu.

    Analowa mu Yerusalemu ndipo anthu anasangalala

  • Anaphunzitsa m’kachisi

  • Mateyu 21:1-11, 14-17

  • Maliko 11:1-11

  • Luka 19:29-44

  • Yohane 12:12-19

MADZULO

Bwererani koyambirira

Nisani 10

MADZULO

  • Anakhala usiku wonse ku Betaniya

M’MAWA

  • Yesu akugubuduza matebulo a anthu osintha ndalama m’kachisi.

    Analawirira kupita ku Yerusalemu

  • Anathamangitsa ogulitsa malonda m’kachisi

  • Yehova analankhula kuchokera kumwamba

  • Mateyu 21:18, 19; 21:12, 13

  • Maliko 11:12-19

  • Luka 19:45-48

  • Yohane 12:20-50

MADZULO

Bwererani koyambirira

Nisani 11

MADZULO

M’MAWA

  • Jesus talking to some of his apostles on the Mount of Olives. The temple stands in the background.

    Anaphunzitsa m’kachisi pogwiritsa ntchito mafanizo

  • Anadzudzula Afarisi mwamphamvu

  • Anaona mkazi wamasiye akuponya timakobidi tiwiri

  • Paphiri la Maolivi, ananeneratu za kuwonongedwa kwa Yerusalemu ndi chizindikiro cha kukhalapo kwake

  • Mateyu 21:19–25:46

  • Maliko 11:20–13:37

  • Luka 20:1–21:38

MADZULO

Bwererani koyambirira

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena