Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g05 4/8 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2005
  • Nkhani Yofanana
  • Achichepere Amakono Akumana ndi Zitokoso za m’ma 1990
    Galamukani!—1990
  • Kodi Achinyamata Amakumana ndi Mavuto Otani?
    Galamukani!—2009
  • Achichepere Amakono Zitokoso Zimene Amakumana Nazo
    Galamukani!—1990
  • Achinyamata, Yendani Moyenera Yehova
    Nsanja ya Olonda—2003
Onani Zambiri
Galamukani!—2005
g05 4/8 tsamba 1-2

Zamkatimu

April 8, 2005

Kuthandiza Achinyamata Amene Ali Pamavuto

Akatswiri ambiri akunena kuti achinyamata a masiku ano ali ndi mavuto ambiri. Nkhani za m’magazini ino zikufotokoza zifukwa zina zimene zikuchititsa achinyamata kukhala pamavuto ndiponso zili ndi malangizo othandiza achinyamata ndi makolo.

3 Zinthu Sizikuwayendera Bwino Achinyamata

5 Mavuto Amene Achinyamata Akukumana Nawo Masiku Ano

9 Zimene Zingathandize Achinyamata Masiku Ano

12 Kodi Mumayendetsa Galimoto Mbali Iti ya Msewu?

18 Oonerera Opanda Chitetezo

19 N’chifukwa Chiyani Mapiri Ali Ofunika kwa Ife?

21 Mapiri Ali Pangozi

27 Kodi Ndani Adzapulumutse Mapiri?

28 Achinyamata Akufunsa Kuti . . .

Ndizigwira Ntchito Yamanja Chifukwa Chiyani?

31 Kodi Akaidi Angatheke Kuwasintha?”

32 Mayankho Othandiza a Mafunso Amene Mwakhala Mukufunsa

Kodi Mulungu Amavomereza Maukwati a Amuna Okhaokha Kapena Akazi Okhaokha? 16

Nkhani imeneyi yabutsa mkangano waukulu. Kodi Baibulo limapereka malangizo omveka bwino otani pa nkhani imeneyi?

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

Photo by Chris Hondros/Getty Images

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena