Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 2/09 tsamba 27-31
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
  • Galamukani!—2009
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi pa Chithunzichi Pakusowa Chiyani?
  • Kuchokera M’magazini Ino
  • Zithunzi Zoti Ana Apeze
  • Kodi Mumawadziwa Bwino Aneneri?
  • MAYANKHO A MAFUNSO A PA TSAMBA 31
  • Zoti Banja Likambirane
    Galamukani!—2010
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2009
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2008
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2008
Onani Zambiri
Galamukani!—2009
g 2/09 tsamba 27-31

Kodi Mungayankhe Bwanji?

Kodi pa Chithunzichi Pakusowa Chiyani?

Werengani 1 Mafumu 18:19-24, 30-40. Tsopano yang’anani pachithunzicho. Kodi ndi zinthu ziti zimene zikusowapo? Lembani mayankho anu m’mizere ili m’munsiyi.

1. ․․․․․

2. ․․․․․

3. ․․․․․

KAMBIRANANI:

N’chifukwa chiyani Yehova analandira nsembe ya Eliya? Kodi Yehova amalandira nsembe zotani kuchokera kwa atumiki ake masiku ano?

Kuchokera M’magazini Ino

Yankhani mafunsowa, ndipo lembani vesi kapena mavesi a m’Baibulo omwe akusowapo.

TSAMBA  7 Kodi Yehova walenjeka dzikoli pa chiyani? Yobu 26:․․․

TSAMBA 9 Kodi ndi ntchito za ndani zimene zinapangidwa mwanzeru? Masalmo 104:․․․

TSAMBA  13 Kodi tingatani kuti tisankhe moyo? Deuteronomo 30:․․․

TSAMBA  20 Kodi Yehova amapereka chiyani munthu akamapemphera kwa Iye ndi mtima wonse? Afilipi 4:․․․

Zithunzi Zoti Ana Apeze

Kodi mungathe kupeza zithunzi izi m’magazini ino? Fotokozani zimene zikuchitika pa chithunzi chilichonse.

Kodi Mumawadziwa Bwino Aneneri?

4. ․․․․․

Mfumu ya Yuda dzina lake Yoasi itachita zoipa, kodi ndi mneneri uti amene anaidzudzula?

ZOKUTHANDIZANI: Werengani 2 Mbiri 24:20-22.

5. ․․․․․

Mfumu Yoasi inapha mneneriyu chifukwa choidzudzula. Kodi izi zikutanthauza kuti Yehova sanasangalale ndi zimene mneneriyu anachita?

ZOKUTHANDIZANI: Werengani Luka 11:50, 51.

KAMBIRANANI:

N’chifukwa chiyani simuyenera kudandaula anthu akamakuzunzani chifukwa choti mumamvera Yehova?

ZOKUTHANDIZANI: Werengani Mateyo 5:11, 12 ndi 1 Petulo 4:14.

◼ (Mayankho ali pa tsamba 27)

MAYANKHO A MAFUNSO A PA TSAMBA 31

1. Ng’ombe yoti iperekedwe nsembe.

2. Ngalande yodzaza madzi.

3. Aneneri a Baala 450 komanso ena ambirimbiri amene anabwera kudzaonera.

4. Zakariya mwana wa Yehoyada.

5. Ayi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena