Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 4/09 tsamba 14-31
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
  • Galamukani!—2009
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Chalakwika N’chiyani Pachithunzichi?
  • Kuchokera M’magazini Ino
  • Zithunzi Zoti Ana Apeze
  • Kodi Mumadziwa Chiyani za Aneneri?
  • MAYANKHO A MAFUNSO A PATSAMBA 31
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2008
  • Mulungu Amadana Ndi Zinthu Zopanda Chilungamo
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2009
  • Kodi Mungayankhe Bwanji?
    Galamukani!—2009
Onani Zambiri
Galamukani!—2009
g 4/09 tsamba 14-31

Kodi Mungayankhe Bwanji?

Kodi Chalakwika N’chiyani Pachithunzichi?

Werengani Yoswa 2:15-18; 6:15-21; 7:1, 20, 21. Ndiyeno onani chithunzichi. N’chiyani chalakwika pachithunzichi? Lembani mayankho anu m’mizere yomwe ili m’munsiyi.

1. ․․․․․

2. ․․․․․

3. ․․․․․

4. ․․․․․

KAMBIRANANI:

Kodi Mulungu amamuona bwanji munthu amene watenga zinthu zomwe si zake?

Kuchokera M’magazini Ino

Yankhani mafunsowa, ndipo lembani vesi kapena mavesi a m’Baibulo omwe akusowapo.

TSAMBA 5 Kodi Danieli ankadziwika chifukwa chiyani ? Danieli 6:․․․

TSAMBA 6 Kodi anthu ayenera kuzindikira chiyani za inuyo? Afilipi 4:․․․

TSAMBA 28 Kodi ukwati uyenera kukhala wotani pakati pa onse? Aheberi 13:․․․

TSAMBA 28 Kodi chilakolako chikatenga pathupi, chimabala chiyani? Yakobe 1:․․․

Zithunzi Zoti Ana Apeze

Kodi mungapeze zithunzi izi m’magazini ino? Fotokozani zimene zikuchitika pachithunzi chilichonse.

Kodi Mumadziwa Chiyani za Aneneri?

Werengani 2 Mbiri 18:1–19:3. Ndiyeno yankhani mafunso otsatirawa.

5. ․․․․․

Tchulani dzina la mneneri amene mfumu Ahabu ankadana naye?

6. ․․․․․

N’chifukwa chiyani Ahabu ankadana ndi mneneri ameneyu?

7. ․․․․․

Kodi mneneriyu anamuuza chiyani Ahabu ndipo Ahabu anatani?

KAMBIRANANI:

Kodi ndi panthawi iti imene mungafunikire kulimba mtima ngati mneneriyu?

◼ Mayankho ali pa tsamba 14

MAYANKHO A MAFUNSO A PATSAMBA 31

1. Makoma a Yeriko anagwa Aisiraeli asanaukire mzindawo.

2. Chingwe chimene Rahabi anatsitsa chinali chofiira osati cha buluu.

3. Akani anaba malaya, chikute cha golide, masekeli a siliva, osati fano

4. Sanaukire usiku.

5. Mikaya.

6. Ananena zoti Yehova aweruza Ahabu.

7. Kuti Ahabu akagonja ku nkhondo. Ahabu anatsekera Mikaya m’ndende.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena