Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 6/10 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2010
  • Nkhani Yofanana
  • Kupanikizika Maganizo Kwabwino ndi Koipa
    Galamukani!—1998
  • Zimene Tingachite Kuti Tisamapanikizike Kwambiri
    Galamukani!—2010
  • Kusowa Mtendere Chifukwa cha Moyo Wopanikizika
    Galamukani!—2005
  • Kupanikizika N’koopsa Kwambiri
    Galamukani!—2010
Onani Zambiri
Galamukani!—2010
g 6/10 tsamba 1-2

Zamkatimu

June 2010

Zimene Mungachite Ngati Mumapanikizika Kwambiri

Akuti kupanikizika n’koopsa kwambiri kuposa chinthu china chilichonse pa moyo wathu. Werengani nkhanizi kuti mudziwe zimene thupi lathu limachita tikapanikizika, ndiponso zimene tingachite kuti tisamapanikizike kwambiri.

3 Kupanikizika N’koopsa Kwambiri

4 Kupanikizika Kumayambitsa Mavuto Aakulu

6 Zimene Tingachite Kuti Tisamapanikizike Kwambiri

10 Mbalame Zampala Zimene Zinaletsedwa Kuulukira Kutali

12 Zimene Achinyamata Amadzifunsa

N’chifukwa Chiyani Ndiyenera Kusamalira Thanzi Langa?

15 Panagona Luso!

Kuwala kwa Ziphaniphani

16 Njanji Yochoka Kunyanja Kukafikanso Kunyanja

22 Zimene Baibulo Limanena

Kodi Atsogoleri Achipembedzo Ayenera Kulipidwa Akachititsa Mwambo Winawake?

27 Tetezani Banja Lanu ku Matenda a Chimfine

30 Zochitika Padzikoli

31 Zoti Banja Likambirane

32 “ Khalanibe pa Ubwenzi ndi Yehova”

Matenda Ofooketsa Mafupa Amayamba Mosaonekera 19

M’mayiko a ku Ulaya, pa masekondi 30 alionse, munthu mmodzi amathyoka fupa chifukwa cha matenda ofooketsa mafupa. Ku United States, akuti mkazi mmodzi pa akazi awiri alionse a zaka zoposa 50, akhoza kudzathyoka fupa pa nthawi inayake pa moyo wake chifukwa cha matendawa. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene mungachite kuti mupewe matendawa.

Ndinasiya Ntchito ya Ndalama Zambiri 24

Martha anatchuka ndiponso analemera chifukwa cha ntchito yoimba koma kenako anasiya. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene zinachititsa kuti asiye ntchitoyi komanso zimene zinamuthandiza kuti akhale wosangalala.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena