Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 11/10 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2010
  • Nkhani Yofanana
  • Diso la Nkhanu Yooneka Ngati Chiswamphika
    Galamukani!—2010
  • Anthu Okhulupirira Kuti Kulibe Mulungu Ali pa Kampeni
    Galamukani!—2010
  • Makadamiya Mtedza Wokoma wa ku Australia
    Galamukani!—2010
  • Kodi Mukanena Chiyani kwa Wosakhulupirira Mulungu?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1999
Onani Zambiri
Galamukani!—2010
g 11/10 tsamba 1-2

Zamkatimu

November 2010

Anthu Okhulupirira Kuti Kulibe Mulungu Ali Pa Kampeni

Ena mwa anthu otchuka kwambiri padzikoli amene amakhulupirira zoti kulibe Mulungu ali pa kampeni. Cholinga chawo n’chakuti anthu enanso ngati inuyo muyambe kukhulupirira zomwezo. Koma kodi mfundo zawo n’zomveka?

3 Anthu Okhulupirira Kuti Kulibe Mulungu Ali pa Kampeni

4 Kodi Pali Umboni Wasayansi Wotsimikizira Zoti Kulibe Mulungu?

6 Kodi Zinthu Zingayambe Kuyenda Bwino Padzikoli Patakhala Kuti Palibe Zipembedzo?

8 “ Ndinakulira M’banja Losakhulupirira Kuti Kuli Mulungu”

10 Zimene Amachita ku Mumbai Kuti Azidya Chakudya Chotentha Kuntchito

13 Kodi Gasi Amachokera Kuti?

19 Malangizo Omwe Angatithandize Kulamulira Lilime Lathu

20 Zimene Baibulo Limanena

Kodi Tiyenera Kupemphera kwa “Oyera”?

22 Makadamiya—Mtedza Wokoma wa ku Australia

24 Panagona Luso!

Diso la Nkhanu Yooneka Ngati Chiswamphika

25 “ Simunataye Mtima”

30 Zochitika Padzikoli

31 Zoti Banja Likambirane

32 Kodi N’chifukwa Chiyani Muyenera Kudziwa Uthenga wa M’Baibulo?

Buku Limene Mungathe Kulikhulupirira—Gawo 1 15

Nkhaniyi ndi yoyamba pa nkhani 7 zotsatizana zimene zizifotokoza mbiri ndi ulosi wa m’Baibulo. Cholinga cha nkhanizi ndi kukuthandizani kuona kuti Baibulo ndi lolondola komanso lodalirika.

Kodi Ndisiye Sukulu? 26

Kodi muyenera kusiyira pati sukulu? Kodi zolinga zanu pa nkhani ya maphunziro ndi zotani? Nkhaniyi ikuthandizani kusankha zinthu mwanzeru.

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

Photograph taken by courtesy of the British Museum

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena