Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g19 No. 3 tsamba 14-15
  • Palibenso Buku Lothandiza Kwambiri Kuposa Baibulo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Palibenso Buku Lothandiza Kwambiri Kuposa Baibulo
  • Galamukani!—2019
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • MABAIBULO OMWE AMASULIRIDWA KOMANSO KUFALITSIDWA
  • KUTI MUDZIWE ZAMBIRI
  • A MBONI ZA YEHOVA AMAKHULUPIRIRA BAIBULO
  • BAIBULO LA DZIKO LATSOPANO
  • Anthu Miyandamiyanda Padziko Lonse Akuyamikira Baibulo la New World Translation
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Yehova Amalankhula Nafe
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Chochitika Chosaiŵalika kwa Okonda Mawu a Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1999
  • Baibulo Lakumana ndi Zambiri
    Galamukani!—2007
Onani Zambiri
Galamukani!—2019
g19 No. 3 tsamba 14-15
Mzimayi akuwerenga Baibulo

Palibenso Buku Lothandiza Kwambiri Kuposa Baibulo

Baibulo ndi buku lomwe limafalitsidwa komanso kumasuliridwa m’zinenero zambiri kuposa buku lina lililonse. Ndiponso mfundo zake zathandiza anthu ambiri kuposa mabuku ena. Mwachitsanzo taganizirani izi:

MABAIBULO OMWE AMASULIRIDWA KOMANSO KUFALITSIDWA

Milu ya Mabaibulo
  • 96.5% ya anthu padzikoli ali nalo

  • LIKUPEZEKA m’zinenero 3,350 (LONSE KAPENA MBALI YAKE)

  • 5,000,000,000: Chiwerengero cha mabaibulo amene afalitsidwa. Chiwerengerochi n’choposa mabuku ena onse omwe afalitsidwapo

KUTI MUDZIWE ZAMBIRI

PITANI PAWEBUSAITI YATHU YA JW.ORG. PAWEBUSAITIYI MUKHOZA:

  • Kuwerenga Baibulo (lomwe likupezeka m’zinenero zoposa 260)

  • Kupanga dawunilodi Baibulo

  • Kupeza mayankho a mafunso anu

  • Kuwerenga nkhani zosonyeza mmene Baibulo lathandizira anthu kukhala ndi moyo wabwino

  • Kuphunzira Baibulo pa intanetia

  • Kupempha kuti munthu aziphunzira nanu Baibulo

A MBONI ZA YEHOVA AMAKHULUPIRIRA BAIBULO

A MBONI ZA YEHOVA AMADZIPEREKA KUGWIRA NTCHITO YOMASULIRA KOMANSO KUFALITSA BAIBULO.

Pamunsipa pali Mabaibulo omwe takhala tikufalitsa m’mbuyomu.

  • American Standard Version of 1901

  • The Bible in Living English by Byington

  • The Emphatic Diaglott

  • King James Version

  • Revised Standard Version

  • Tischendorf’s New Testament

BAIBULO LA DZIKO LATSOPANO

Girafu yosonyeza mmene Baibulo la Dziko Latsopano lakhala likufalitsidwira kuchokera mu 1950 mpaka mu 2020
  • 180+ Zinenero (LONSE KAPENA MBALI YAKE)

  • 227 MILLION KUCHULUKA KWA MABAIBULO A DZIKO LATSOPANO OMWE AKHALA AKUFALITSIDWA KUCHOKERA MU 1950

a Panopa munthu akhoza kuphunzira m’Chingelezi komanso m’Chipwitikizi. Zinenero zina zibwera m’tsogolomu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena