Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • le tsamba 6-7
  • Kodi N’chifukwa Ninji Munthu Amafa?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi N’chifukwa Ninji Munthu Amafa?
  • Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
  • Nkhani Yofanana
  • Mulungu ndi Wamkulu Kuposa Aliyense
    Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso
  • Kodi Moyo Unali Wotani m’Paradaiso?
    Mverani Mulungu Kuti Mudzapeze Moyo Wosatha
  • Pali Wina Wokulirapo
    Kumamumvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo
  • Chigawo 3
    Mverani Mulungu
Onani Zambiri
Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
le tsamba 6-7

Kodi N’chifukwa Ninji Munthu Amafa?

8 Yehova anafuna kuti munthu apange dziko lonse lapansi kukhala lokongola—paradaiso kuti onse asangalale nalo.—Genesis 1:28

Anthuwo akanatha kukhala ndi moyo kosatha akadakhala kuti Adamu ndi Hava adamvera Yehova. Iwo anauzidwa kusadya za mumtengo wakudziŵitsa zabwino ndi zoipa.—Genesis 2:15-17

9 Mngelo wina anakhala woipa nagwiritsira ntchito chinjoka kuchititsa Hava ndi Adamu kusamvera Mulungu.—Genesis 3:1-6

10 Mngelo amene ananyenga Hava anayamba kutchedwa ‘njoka yokalambayo, Mdierekezi ndi Satana.’—Chivumbulutso 12:9

11 Yehova anathamangitsa m’paradaiso aŵiri osamverawo.—Genesis 3:23, 24

12 Adamu ndi Hava anabala ana, koma banja lonse silinali lokondwa.—Genesis 3:17, 18

13 Iwo anayenera kukalamba ndi kufa, monga momwe Yehova anali atanenera.—Genesis 3:19; Aroma 5:12

14 Chotero iwo anafa mofanana ndi nyama.

Miyoyo yonse pa dziko lapansi imafa.—Mlaliki 3:18-20; Ezekieli 18:4

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena