Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • le tsamba 18-21
  • Boma Lakumwamba Lidzetsa Madalitso pa Dziko Lapansi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Boma Lakumwamba Lidzetsa Madalitso pa Dziko Lapansi
  • Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
  • Nkhani Yofanana
  • Boma Limene Lidzabweretsa Paradaiso
    Boma Limene Lidzabweretsa Paradaiso
  • Kodi Ufumu wa Mulungu N’chiyani?
    Zimene Baibulo Limaphunzitsa
  • Kodi Chifuno cha Mulungu cha Dziko Lapansi N’chiyani?
    Kodi Mulungu Amafunanji kwa Ife?
  • Zokhudza Ufumu wa Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2008
Onani Zambiri
Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
le tsamba 18-21

Boma Lakumwamba Lidzetsa Madalitso pa Dziko Lapansi

41 Yehova anapanga Yesu kukhala Mfumu kumwamba.—Yesaya 9:6; Danieli 7:13, 14; Machitidwe 2:32-36

42 Iye adzalamulira pa dziko lonse lapansi.—Danieli 7:14; Mateyu 28:18

43 Kodi mukukumbukira chimene chidzachitikira anthu oipa?—Salmo 37:9, 10; Luka 13:5

44 Kodi mukukumbukira dzina la mngelo woyambirira amene anachimwa? Yesu adzam’chotsa ndi angelo ena oipa. Mafano awo ndi zifanizo zidzawonongedwa.—Ahebri 2:14; Chivumbulutso 20:2, 10

45 Yesu adzachita zinthu zambiri zabwino kwa anthu omvera.—Ahebri 5:9

46 Palibe aliyense amene adzadwalanso.—Yesaya 33:24; Chivumbulutso 22:1, 2

Kodi mukukumbukira mmene Yesu anachiritsira anthu odwala?

47 Aliyense adzakhala ndi zinthu zabwino.—Yesaya 65:17, 21-23

48 Mulungu amakumbukira ngakhale anthu amene afa. Iye adzagwiritsira ntchito Yesu kuwadzutsira ku moyo kachiŵirinso. Kumeneku kumatchedwa chiukiriro.—Yohane 5:28, 29; 11:25

49 Anthu onse oipa ataphedwa, palibe amene adzafanso. Ngakhale nyama zakuthengo sizidzakhala zoopsa. Aliyense adzakhala wachimwemwe kosatha.—Chivumbulutso 21:4; Yesaya 65:25; Salmo 37:11, 29

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena