Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 50
  • Kuyankha Chikondi cha Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kuyankha Chikondi cha Mulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kulani M’chikondi
    Nsanja ya Olonda—2001
  • “Pitirizani Kusonyeza Chikondi”
    Yandikirani Yehova
  • Kondani Mulungu Amene Amakukondani
    Nsanja ya Olonda—2006
  • “Uzikonda Yehova Mulungu Wako”
    Nsanja ya Olonda—2014
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 50

Nyimbo 50

Kuyankha Chikondi cha Mulungu

(1 Yohane 4:11)

1. Inu ndinu Mulungu; Timkonda mtima wonse

Yehova wotamandikanu.

Titama dzina lanu, Mawu anu mwa zimene

tiphunzira njira zanu.

Musonyeza chifundo, Muchita molungama;

Musonyeza mphamvu ndi nzeru.

Tidziŵa kuti tikakhala owona mtima,

Mudzatipatsa madalitso.

2. Munatikonda ife; Nafe tikukondani

Inu kuchokera mumtima.

Kuyeretsa dzinalo, Kuvumbula chikondi chanu,

Kristu ’nadza ndi moyo.

Palibenso chikondi Kuti wina apatsa

Moyo wake mongatu nsembe.

Kuti ife tisawonongeke timamvera

Uphungu ndi chilangizocho.

3. Sitidzapatutsidwa Pautumiki wathu;

Tidzanenabe chowonadi.

Mwautumiki wathu Tidzamkabe tikwanitsa

chikondi kwa anthu onse.

Pakumatumikira Chikondano chathuchi

Chivumbula otsata Kristu.

Zinthutu zake za Ufumu tisamalira;

Poyembekezera lonjezo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena