Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 57
  • Anthu Achimwemwe a Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Anthu Achimwemwe a Yehova
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Thaŵirani ku Ufumu wa Mulungu!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Lonjezo la Mulungu la Paradaiso
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 57

Nyimbo 57

Anthu Achimwemwe a Yehova

(Salmo 89:15)

1. Achimwemwe ndi odziŵatu lipenga,

Odziŵa cho’nadi, Adzadalitsidwa.

Adzayendabe mukuunika kwa inu;

Apeza chimwemwe potumikira.

(Korasi)

2. Makamu a Satana apondereza;

Ntchito zichuluke; Thamo limveketu.

M’lungu wakonza pothaŵirapo ofatsa;

Ateteza ofuna chilungamo.

(Korasi)

3. Popatuka ena tisataye mtima.

Ngakhale akana, Tidzakhala maso.

Tipiriretu pomasonyeza umphumphu;

Popeza M’lungu amayamikira.

(KORASi)

Chifundo chanu, muchisonyeza

Kwa olengezabe dzina lanulo.

Mwa Mawu anu awona cho’nadi,

Asonyeza chikhulupiriro.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena