Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 83
  • Chifukwa cha Kukondwera cha Ziyoni

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chifukwa cha Kukondwera cha Ziyoni
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Mtundu Woyera wa Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Dalitsani Ubale Wathu Wachikristu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tizichita Zinthu Zogwirizana Ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Zochita Zathu Zizigwirizana ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 83

Nyimbo 83

Chifukwa cha Kukondwera cha Ziyoni

(Yesaya 66:8)

1. M’lungu ali ndi mtundu;

Wobadwatu lero.

“Dziko” linakhalapo

Sitidzaliranso.

Ziyoni wakumwamba—

Anabala ana

A’muna amenetu

Adziŵitsa M’lungu.

(Korasi)

2. Kubadwa kwa mtunduwu

Kwadzetsa chimwemwe.

Usamalira zinthu

Ndi nkhosa za M’lungu.

E, ana a Ziyoni

Awopa mawuwo.

Alalika molimba.

Samawopa chinthu.

(Korasi)

3. Chiri chifuno cha

Ya Mitundu iwope.

Mitundu yosankhidwa

Imka ku Ziyoni.

Ndimwaŵi wa padera

Kukwezetsa mbiri,

Ndi kumulambiradi,

Atchula dzinalo.

(KORASi)

Kodwerani ndi Ziyoni mmwamba!

Chikondi cha Ya nchachikuludi!

Ana padziko atumikira,

pagomelo la Ya aseyama.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena