Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 114
  • Chikondi cha Mulungu Chokhulupirika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chikondi cha Mulungu Chokhulupirika
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Chikondi cha Mulungu N’chosatha
    Imbirani Yehova
  • Chikondi Chokhulupirika cha Mulungu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kodi Timapindula Bwanji ndi Chikondi Chokhulupirika cha Yehova?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Dzina la Atate Wathu
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 114

Nyimbo 114

Chikondi cha Mulungu Chokhulupirika

(Yesaya 55:1-3)

1. M’lungu ndi chikondi.

Chimatikondweretsa.

Anatuma Mwanake,

Anapereka dipo,

Tipeze chilungamo,

Ndi moyo wamuyaya.

(Korasi)

2. M’lungu ndi chikondi.

Ntchitozo nza umboni.

Amatikonda ife,

Ufumu ndi wa Kristu

Kukwanitsa lumbiro.

Ufumuwo wabadwa.

(Korasi)

3. M’lungu ndi chikondi.

Natumiza mtendere.

Natipatsa ‘kapolo,’

Ndi kupatsidwa ntchito,

Yakudziŵitsa dzina,

La Yehova Mulungu.

(Korasi)

4. M’lungu ndi chikondi.

Tisonyeze chikondi.

Ndi kuthandiza ena,

Kupeza chilungamo.

Tilalike ponsepo,

Chitonthozo padziko.

(KORASI)

Inu nonse aludzu,

Idzani mudzamwetu,

Madziwo kwaulere;

Chifundo cha M’lungu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena