Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 154
  • Yehova, Mlengi Wathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova, Mlengi Wathu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ufumu wa Yehova Wayamba Kulamulira
    Imbirani Yehova
  • Abale Ambirimbiri
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khamu la Abale
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 154

Nyimbo 154

Yehova, Mlengi Wathu

(Yesaya 42:5)

1. Yehova Mfumu anapanga dzikoli.

Anawapatsa anthu kukhalamo.

Angelo zikwizikwi anafuula

Mulungu atatha; linakongola.

2. Dzikoli lidzakhala Paradaiso.

Ndicho chifuno chake cha Yehova.

Tchimo linayamba ndi kupandukira.

Lidzatha mwamsanga; timakondwera.

3. Kudza kwa Ufumu kudzakonza zinthu.

Timayembe kezeradi nthaŵiyo.

Mokondwera timalengeza mbiriyo,

Kuŵalitsira anthu chowonadi.

4. Tiyang’ana kwa Yehova mwachikondi,

Ndiye Mlengi wathu, wotamandidwa.

Anapangira anthu zonse mwanzeru!

Timtame timtumikire ndi mtima.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena