Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 167
  • Tiyamika Wotipatsa Moyo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tiyamika Wotipatsa Moyo
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Kristu Chitsanzo Chathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pemphero la Mtumiki wa Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuyenda m’Dzina la Mulungu Wathu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tiyenera Kuyembekezera Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 167

Nyimbo 167

Tiyamika Wotipatsa Moyo

(Salmo 36:9)

1. Zikomodi Ya wakumwambanu.

Tingachitenji kukutamani?

Mosamalitsatitsate Kristu,

Titukulira manja m’mwambamo.

2. Tiri okondwa Mfumu yosatha;

M’mwamba ndi dziko zitumikira.

Tisiya zonse tirinazozi,

M’kulambiridwa, ndi malamulo.

3. Munakhazika Ufumu wanu;

Tiri nanu unansi wabwino.

Tidikiranu nzeru yanuyo,

Kutitu ife tilambire’nu.

4. Titumikenu mosangalala,

Tidziŵitse chowonadi chanu.

Dalitsanitu zochita zathu,

Mzimu wanuwo utilimbitse.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena