Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 176
  • Kulandira Mfumu Yakudzayo!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kulandira Mfumu Yakudzayo!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Landiranani’!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo Yachilakiko
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tizilandilana
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Landiranani
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 176

Nyimbo 176

Kulandira Mfumu Yakudzayo!

(Salmo 24:7)

1. Nthaŵi yafika yakuti tilandire

M’lungu Wamphamvuyonse mwini zinthu.

Iye ndi Mwanayo aika mitundu,

Ndipo miyamba ikumveka ndi nyimbo yankhondo.

‘Dzutsani mitu, O zipata’ mokondwa;

Mfumu yaikulu idzapambana.

Nthaŵi ya magulu a Yehova yadza

Kudzetsera anthu Zaka Chikwizo.

Adzasonyeza mphamvu mu Ufumuwo,

Ulamuliro wake udzafalikira.

2. Ambuye Mfumu, Wamkuludi, Yehova,

Wadzetsa Ufumu womwe sudzatha.

Akuyenereradi kulandiridwa;

Tidziŵitse Mfumuyo kuti timaitamanda.

Zitseguketu, zipata! Mbiri yadza;

Nchikondwerero kuimba limodzi.

‘Yehova ngwamphamvu wamkulu munkhondo.’

Timumvetsere ndi kudza ndi mphatso,

Nthaŵi yadza kudalitsa oyanjidwa.

‘Tikulandirenitu!’ Mfumu yakudzanu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena