Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 90
  • Ulemerero Umene Umabwera Chifukwa cha Imvi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ulemerero Umene Umabwera Chifukwa cha Imvi
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Imvi Ndi Chisoti cha Ulemerero
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Mulungu Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova
  • Yehova, Nyonga Yathu ndi Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 90

Nyimbo 90

Ulemerero Umene Umabwera Chifukwa cha Imvi

Losindikizidwa

(Miyambo 16:31)

1. Pakati pathu pali

Achikulire.

Akukondabe M’lungu

Sanamusiye.

Ena imfa ya mnzawo

Ikuwawawa.

Tate atonthozeni,

N’kuwalimbitsa.

(KOLASI)

Mumakumbukira

Zochita zawo.

Tate auzeni:

“Mwachita bwino.”

2. Imvi za olungama

Ndi zokongola.

Zimasangalatsadi

Tate Yehova.

Ife tikumbukire

Pa nthawi ina

Pa unyamata wawo

Ankayesetsa.

(KOLASI)

Mumakumbukira

Zochita zawo.

Tate auzeni:

“Mwachita bwino.”

(Onaninso Sal. 71:9, 18; Miy. 20:29; Mat. 25:21, 23; Luka 22:28; 1 Tim. 5:1.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena