Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 113
  • Tikuyamikira Mulungu Kuti Anatipatsa Mawu Ake

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikuyamikira Mulungu Kuti Anatipatsa Mawu Ake
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tikuthokoza Mulungu Potipatsa Mawu Ake
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kodi Mzimu wa Munthu Sufa?
    Nsanja ya Olonda—2007
  • “Muziyamika pa Chilichonse”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Khulupirirani Mawu a Yehova
    Nsanja ya Olonda—2005
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 113

Nyimbo 113

Tikuyamikira Mulungu Kuti Anatipatsa Mawu Ake

Losindikizidwa

(Afilipi 2:16)

1. Yehova Atate, tikuyamika

Chifukwa mawu anu mwatipatsa.

Munauzira anthu kulemba za inu.

Malemba ’matitsogolera ndithu.

2. Aneneri anu anali anthu,

Ankamvadi mmene timamveratu.

Ndipo za moyo wawo tikamaphunzira

Timakhala anthu olimba mtima.

3. Mawu anu amatikhudza mtima.

Moyo ndi mzimu amalekanitsa.

Afufuza zolinga za mumtima wathu.

Atithandiza kukhala ndi nzeru.

(Onaninso Sal. 119:16, 162; 2 Tim. 3:16; Yak. 5:17; 2 Pet. 1:21.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena