Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mb phunziro 1
  • Phunziro 1

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Phunziro 1
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Mapiko a Gulugufe
    Galamukani!—2014
  • Mapiko a Gulugufe
    Galamukani!—2012
  • Luso la Gulugufe Woyera Lotha Kuimitsa Mapiko Ake Ngati V
    Kodi Zinangochitika Zokha?
Onani Zambiri
Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
mb phunziro 1

Phunziro 1

Losindikizidwa

Chivumbulutso 4:11

Kodi ndani analenga dziko lapansili?

Kodi ndani analenga nyanja?

Kodi ndani analenga iweyo ndi ine?

Kodi ndani analenga gulugufe wa mapiko okongola chonchi?

Yehova Mulungu ndi amene analenga zinthu zonse.

ZOTI MUCHITE

Mwana wanuyo muwerengereni:

Chivumbulutso 4:11

Muuzeni mwanayo kuti aloze:

Nyenyezi Mitambo Dzuwa

Boti Dziko Nyumba

Nyanja Gulugufe

Mufunseni mwana wanu kuti:

Kodi dzina la Mulungu ndani?

Kodi Yehova amakhala kuti?

Kodi Yehova analenga zinthu ziti?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena