Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mb phunziro 2
  • Phunziro 2

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Phunziro 2
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Anthu 8 Anapulumuka
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Kodi Galu Wanu Sangavulaze Ana?
    Galamukani!—1997
  • Nowa Akhoma Chingalawa
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
Onani Zambiri
Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
mb phunziro 2

Phunziro 2

Losindikizidwa

Genesis 7:7-10; 8:15-17

Waziona nyama zimene zili pafupi ndi chingalawa cha Nowa?

Kodi ndi nyama ziti zimene zimalira kuti moo? Nanga ndi ziti zimene zimauwa?

Chingalawa cha Nowa chinapulumutsa nyama zonse, zazifupi ndi zazitali zomwe.

ZOTI MUCHITE

Mwana wanuyo muwerengereni:

Genesis 7:7-10; 8:15-17

Muuzeni mwanayo kuti aloze:

Chimbalangondo Galu Njovu

Kadyansonga Mkango Nyani

Nkhumba Nkhosa

Mbidzi Utawaleza

Muuzeni mwanayo kuti ayerekezere mmene nyama izi zimalirira:

Galu Mbuzi Tambala

Nkhumba Ng’ombe

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena