Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • snnw tsamba 6
  • Kufufuza Anthu Okonda Mtendere

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kufufuza Anthu Okonda Mtendere
  • Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Yofanana
  • Kufufuza Anthu Okonda Mtendere
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo wa Mpainiya
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw tsamba 6

Nyimbo 141

Kufufuza Anthu Okonda Mtendere

(Luka 10:6)

  1. Yesu anatilamula kuti

    tiuze anthu uthenga.

    Amve mawu a Yehova.

    Ankakonda nkhosa za Mulungu.

    Ankazifufuza

    mwakhama tsiku lonse.

    Nyumba ndi nyumba, mumsewu

    Timalalika kwa anthu,

    Kuti posachedwa mavuto atha.

    (KOLASI)

    Tifufuze

    okonda mtendere m’dzikoli.

    Tiwapeze

    Ofuna kupulumutsidwa.

    Tifufuze

    Paliponse.

  2. Tifufuzabe anthu mwa khama.

    Alipo ambiri

    omwe tingathe kuwathandiza.

    Poti timawakonda kwambiri,

    Tibwererekonso

    Tikawalimbikitse.

    M’matauni, ndi m’midzinso,

    Tikapeza omvetsera,

    Timasangalala powaphunzitsa.

    (KOLASI)

    Tifufuze

    okonda mtendere m’dzikoli.

    Tiwapeze

    Ofuna kupulumutsidwa.

    Tifufuze

    Paliponse.

(Onaninso Yes. 52:7; Mat. 28:​19, 20; Luka 8:1; Aroma 10:10.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena