Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • lfb tsamba 22-23
  • Mawu Oyamba Gawo 3

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mawu Oyamba Gawo 3
  • Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Nkhani Yofanana
  • Abulahamu Anali “Bwenzi” la Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • Yehova Akhoza Kukhala Mnzanu
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Kodi Abulahamu Anali Ndani?
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Abulahamu Anali Munthu Wachikondi
    Nsanja ya Olonda—2012
Onani Zambiri
Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
lfb tsamba 22-23
Abulahamu akufotokozera Isaki za nyenyezi

Mawu Oyamba Gawo 3

Baibulo limanena kuti Chigumula chitatha, panali anthu ena omwe ankatumikira Yehova. Ena mwa anthuwa anali Abulahamu amene ankadziwika kuti anali mnzake wa Yehova. N’chifukwa chiyani Abulahamu ankatchedwa mnzake wa Yehova? Ngati ndinu kholo, thandizani mwana wanu kudziwa kuti Yehova amamukonda kwambiri ndipo amafunitsitsa kumuthandiza. Mofanana ndi Abulahamu komanso anthu ena okhulupirika monga Loti ndi Yakobo, tingathe kupempha Yehova kuti atithandize. Komanso tizikhulupirira kuti Yehova adzachita chilichonse chimene wanena.

ZIMENE TIPHUNZIRE M’CHIGAWOCHI

  • Tizichita zonse zimene Yehova amatiuza ngakhale zitakhala zovuta

  • Kukhala pa ubwenzi ndi Mulungu ndi chinthu chabwino kuposa chilichonse

  • Yehova amafuna kuti tizikhululukira ena. Amafunanso kuti tikalakwirana, tizikambirana mwamsanga n’kugwirizananso

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena