Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 2
  • ‘Dzina Lanu Ndi Yehova’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Dzina Lanu Ndi Yehova’
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Inu Ndinu Yehova
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 2

NYIMBO 2

‘Dzina Lanu Ndi Yehova’

Losindikizidwa

(Salimo 83:18)

  1. 1. Mulungu woona,

    Mlengi wa zinthu zonse.

    Mulungu wamuyaya,

    Ndinudi Yehova.

    Timasangalala

    Kukhala anthu anu.

    Tilengeze za inu

    Ku mitundu yonse.

    (KOLASI)

    Yehova, Yehova,

    M’lungu ndinu nokha.

    Kumwambako ndi padziko

    Palibenso wina.

    Ndinudi wamphamvuyonse,

    Tidziwitse onse.

    Yehova, Yehova,

    M’lungu wathu ndinu nokha.

  2. 2. Tingathe kukhala

    Chimene mukufuna.

    Mumatithandizatu

    Ndinudi Yehova.

    Mwatipatsa dzina

    Takhala Mboni zanu.

    Ndifedi anthu anu.

    Timakukondani.

    (KOLASI)

    Yehova, Yehova,

    M’lungu ndinu nokha.

    Kumwambako ndi padziko

    Palibenso wina.

    Ndinudi wamphamvuyonse,

    Tidziwitse onse.

    Yehova, Yehova,

    M’lungu wathu ndinu nokha.

(Onaninso 2 Mbiri 6:​14; Sal. 72:19; Yes. 42:8.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena