Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 83
  • “Kunyumba ndi Nyumba”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Kunyumba ndi Nyumba”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Kunyumba Ndi Nyumba”
    Imbirani Yehova
  • “Kumka Kunyumba ndi Nyumba”
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tikulalikira Choonadi Chonena za Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tilalikire Choonadi cha Ufumu
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 83

NYIMBO 83

“Kunyumba ndi Nyumba”

Losindikizidwa

(Machitidwe 20:20)

  1. 1. Ife timalalikira

    Kunyumba ndi nyumba.

    Kulikonse nkhosa za M’lungu

    Zikudyetsedwa.

    Tonse, akulu ndi ana,

    Tikulalikira

    Zoti Ufumu wa M’lungu

    Ukulamulira.

  2. 2. Khomo ndi khomo,

    Tinene za chipulumutso.

    Aitane dzina la M’lungu

    Apulumuke.

    Angaitane bwanji

    Dzina sakulidziwa?

    Choncho kunyumba zawo

    Tikawalalikire.

  3. 3. Khomo ndi khomo,

    Tiyeni tikalalikire.

    Asankhe okha kumvera

    Kapena kukana.

    Koma dzina la Yehova

    Tidzalengezabe.

    Tikamatero,

    Tidzapezadi nkhosa zake.

(Onaninso Mac. 2:21; Aroma 10:14.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena