Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 103
  • Abusa Ndi Mphatso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Abusa Ndi Mphatso
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Abusa Ndi Mphatso za Amuna
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Muzikonda Kwambiri Choonadi Panokha
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 103

NYIMBO 103

Abusa Ndi Mphatso

Losindikizidwa

(Aefeso 4:8)

  1. 1. Yehova watipatsa mphatso,

    Abusa mu mpingo.

    Mwachitsanzo chawo chabwino

    Amatiphunzitsa.

    (KOLASI)

    M’lungu watipatsa akulu

    Omwe timadalira.

    Amadera nkhawa tonsefe

    Ndiye tiziwakonda.

  2. 2. Abusawa ndi achikondi,

    Amaleza mtima.

    Tikapunthwa amathandiza

    Kutitu tichire.

    (KOLASI)

    M’lungu watipatsa akulu

    Omwe timadalira.

    Amadera nkhawa tonsefe

    Ndiye tiziwakonda.

  3. 3. Amatipatsa malangizo,

    Tisasocheretu.

    Tizisangalatsa Mulungu

    Pomutumikira.

    (KOLASI)

    M’lungu watipatsa akulu

    Omwe timadalira.

    Amadera nkhawa tonsefe

    Ndiye tiziwakonda.

(Onaninso Yes. 32:​1, 2; Yer. 3:15; Yoh. 21:​15-17; Mac. 20:28.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena