Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 119
  • Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tikhale ndi Chikhulupiriro
    Imbirani Yehova
  • Tiyenera Kukhala ndi Chikhulupiliro
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Tiwonjezereni Chikhulupiriro”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Muzisonyeza Kuti Mumakhulupirira Malonjezo a Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 119

NYIMBO 119

Tikhale Ndi Chikhulupiriro Cholimba

Losindikizidwa

(Aheberi 10:​38, 39)

  1. 1. Kale Mulungu ankalankhula

    Kudzera mwa aneneri.

    Pano kudzera mwa Mwana wake

    Akuti: ‘Lapanitu.’

    (KOLASI)

    Kodi chikhulupiriro

    Chathu ndi cholimba ndithu?

    Chikakhala chenicheni

    M’pamene tingadzapulumuke.

  2. 2. Timamvera lamulo la Yesu

    Loti tizilalikira.

    Tilengezabe molimba mtima,

    Anthu amve uthenga.

    (KOLASI)

    Kodi chikhulupiriro

    Chathu ndi cholimba ndithu?

    Chikakhala chenicheni

    M’pamene tingadzapulumuke.

  3. 3. Talimbitsa chikhulupiriro

    Sitidzabwerera m’mbuyo.

    Tikudziwa kuti M’lungu wathu

    Adzatipulumutsa.

    (KOLASI)

    Kodi chikhulupiriro

    Chathu ndi cholimba ndithu?

    Chikakhala chenicheni

    M’pamene tingadzapulumuke.

(Onaninso Aroma 10:10; Aef 3:12; Aheb. 11:6; 1 Yoh. 5:4.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena