Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 124
  • Tizikhulupirika Nthawi Zonse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizikhulupirika Nthawi Zonse
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tikhale Okhulupirika Nthawi Zonse
    Imbirani Yehova
  • Kodi Timapindula Bwanji ndi Chikondi Chokhulupirika cha Yehova?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Kodi Mumasangalala ndi Chikondi Chokhulupirika Ngati Mmene Yehova Amachitira?
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Chikondi Chokhulupirika cha Yehova N’chachikulu
    Nsanja ya Olonda—2004
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 124

NYIMBO 124

Tizikhulupirika Nthawi Zonse

Losindikizidwa

(Salimo 18:25)

  1. 1. Tizikhulupirikadi

    Kwa M’lungu ndi kum’konda.

    Tiyesetse kuphunzira

    Malamulo akewo.

    Tikamamvera Mulungu

    Timamusangalatsa.

    Tizikondabe Yehova

    Ndipo tisamusiye.

  2. 2. Tizikhulupirikanso

    Kwa akulu mumpingo.

    Nthawi zonse pamavuto

    Amatisamalira.

    Tiziwapatsa ulemu

    Kuchokera mumtima.

    Tiwamvere nthawi zonse.

    Titumikire nawo.

  3. 3. Tizikhulupirikabe

    Tikamalangizidwa

    Ndi akulu amumpingo.

    Inde tiziwamvera

    Ndipo Yehova Mulungu

    Adzatidalitsadi.

    Tikamakhulupirika,

    Iye azitikonda.

(Onaninso Sal. 149:1; 1 Tim. 2:8; Aheb. 13:17.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena