Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 125
  • “Osangalala Ndi Anthu Achifundo”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Osangalala Ndi Anthu Achifundo”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Achimwemwe, Ngachifundo!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Anthu Achifundo Amakhala Odala
    Imbirani Yehova
  • ‘Atate Wanu Ndi Wachifundo’
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Timatumikira Mulungu “Wachifundo Chochuluka”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 125

NYIMBO 125

“Osangalala Ndi Anthu Achifundo”

Losindikizidwa

(Mateyu 5:7)

  1. 1. Yehova ndi wachifundo,

    Amasonyeza chifundo.

    Iye ndi wokoma mtima.

    Amatisamaliradi.

    Amamvanso mapemphero

    Ochokera kwa olapa.

    Amadziwa ndife fumbi,

    Amatikomera mtima.

  2. 2. Tikachimwa n’kupemphera,

    M’lungu amakhululuka.

    Yesu anatiphunzitsa

    Mmene tingapempherere,

    Muzitikhululukira,

    Takhululukira ena.

    Tisasungenso zifukwa.

    Tidzapezadi mtendere.

  3. 3. Tikapatsa ena mphatso

    Tizisonyeza chifundo.

    Tisamafune kutchuka

    Koma kungowathandiza.

    M’lungu yemwe amaona

    Adzatibwezera ndithu.

    Anthu onse achifundo

    Mulungu amawakonda.

(Onaninso Mat. 6:​2-4, 12-14.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena