Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 127
  • Mtundu wa Munthu Amene Ndiyenera Kukhala

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mtundu wa Munthu Amene Ndiyenera Kukhala
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Mtundu wa Munthu Amene Muyenera Kukhala
    Imbirani Yehova
  • Yehova Akutipempha Kuti: “Mwana Wanga Khala Wanzeru”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Akutipempha Mokoma Mtima Kuti: “Mwana Wanga, Khala Wanzeru”
    Imbirani Yehova
  • Tumikirani Yehova Mokhulupirika
    Nsanja ya Olonda—1992
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 127

NYIMBO 127

Mtundu wa Munthu Amene Ndiyenera Kukhala

Losindikizidwa

(2 Petulo 3:11)

  1. 1. Ndipereke chani kwa inu M’lungu

    Pokuthokozani chifukwa cha moyo?

    Mawu anuwa amandiunikira.

    Ndithandizeni kuti ndidzifufuze.

    (VESI LOKOMETSERA)

    Ndalonjeza kutumikira inu

    Mofunitsitsa ndi moyo wanga wonse.

    Ndinasankha ndekha kutumikira.

    Ndikufuna n’kusangalatseni.

    M’lungu n’thandizeni kudzifufuza

    Kuti ndizichita chifuniro chanu.

    Mumafunatu ndizikhulupirika.

    Ndikufuna ndizikusangalatsani.

(Onaninso Sal. 18:25; 116:12; Miy. 11:20.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena