Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • rr tsamba 108
  • “Nthawi Yobwezeretsa Zinthu Zonse”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Nthawi Yobwezeretsa Zinthu Zonse”
  • Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • MACHITIDWE 3:21
  • “Nthaŵi za Kukonzanso” Zayandikira!
    Nsanja ya Olonda—2000
  • “Ndidzawapatsa Mtima Umodzi”
    Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
  • Mphamvu Zobwezeretsa—Yehova ‘Akupanga Zinthu Zonse Kuti Zikhale Zatsopano’
    Yandikirani Yehova
  • Zaka Chikwi Zopambana Zikuyandikira
    Nsanja ya Olonda​—1990
Onani Zambiri
Yehova Wabwezeretsa Kulambira Koyera
rr tsamba 108

BOKOSI 9E

“Nthawi Yobwezeretsa Zinthu Zonse”

Losindikizidwa

MACHITIDWE 3:21

Pamene mtumwi Petulo ananena za “nthawi yobwezeretsa zinthu zonse,” ankalosera za nthawi yapadera imene inayamba pamene Khristu anakhala pampando wachifumu mpaka kumapeto kwa Ulamuliro wake wa Zaka 1,000.

  1. 1914​—Yesu Khristu wakhala pampando wachifumu kumwamba. Anthu a Mulungu anabwezeretsedwa mwauzimu kuyambira mu 1919

    Masiku Otsiriza

  2. ARAMAGEDO​—Ulamuliro wa Zaka 1,000 wa Khristu unayamba, ndipo “nthawi yobwezeretsa zinthu zonse” inaphatikizapo madalitso amene anthu okhulupirika padziko lapansi analandira

    Ulamuliro wa Zaka 1,000

  3. KUTHA KWA ULAMULIRO WA KHRISTU WA ZAKA 1,000​—Yesu wamaliza ntchito yonse yobwezeretsa zinthu ndipo akupereka Ufumu kwa Atate ake

    Paradaiso Wamuyaya

Banja likucheza m’mbali mwa nyanja m’paradaiso.

ULAMULIRO WA YESU UDZACHITITSA KUTI . . .

  • dzina la Mulungu lilemekezedwe

  • anthu asadzadwalenso

  • achikulire adzakhalenso anyamata

  • amene anafa adzauke

  • anthu okhulupirika adzakhale angwiro

  • dziko lapansi lidzakhale Paradaiso

Bwererani ku mutu 9, ndime 23, 33-39

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena