Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 154
  • Chikondi Sichitha

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chikondi Sichitha
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2019
  • Khalani Ndi Chikondi Chimene Sichitha Konse
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Kulani M’chikondi
    Nsanja ya Olonda—2001
  • “Pitirizani Kusonyeza Chikondi”
    Yandikirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 154

NYIMBO 154

Chikondi Sichitha

Losindikizidwa

(1 Akorinto 13:8)

  1. 1. Tangoonani

    Timakondanadi

    Zomwe n’zosowa m’dzikoli.

    Ndi anzathuwa

    Tikusangalala,

    Sitili mbali ya dziko.

    (KUKONZEKERA KOLASI)

    Chikondi sichithadi.

    Chimapiriratu.

    (KOLASI)

    Chikondichitu,

    Yehova n’chikondi.

    Watipatsa.

    Chikondichitu,

    Ndi chofunikadi.

    Tizikondanabe,

    Ndipo tisasiye

    Chikondichi.

  2. 2. Pena mavuto

    Angatifo’ketse

    N’kuvutika kupirira,

    Koma kupatsa

    Ndi kosangalatsa,

    M’lungu amatitonthoza.

    (KUKONZEKERA KOLASI)

    Chikondi sichithadi.

    Chimapiriratu.

    (KOLASI)

    Chikondichitu,

    Yehova n’chikondi.

    Watipatsa.

    Chikondichitu,

    Ndi chofunikadi.

    Tizikondanabe,

    Ndipo tisasiye.

    (KOLASI)

    Chikondichitu,

    Yehova n’chikondi.

    Watipatsa.

    Chikondichitu,

    Ndi chofunikadi.

    Tizikondanabe,

    Ndipo tisasiye

    Chikondichi,

    Chikondichi,

    Chikondichi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena