Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/09 tsamba 3
  • Bokosi la Mafunso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Bokosi la Mafunso
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Nkhani Yofanana
  • “Kuteteza . . . ndi Kukhazikitsa Mwalamulo Ntchito ya Uthenga Wabwino”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Pitaniko Mwamsanga
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
  • Kutetezedwa Ndi Apolisi N’kolimbitsa Mtima Komanso N’kokayikitsa
    Galamukani!—2002
  • Tizinyamuka Tikangomaliza
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
km 10/09 tsamba 3

Bokosi la Mafunso

◼ Kodi muyenera kuchita chiyani ngati mwaletsedwa kulalikira?

Nthawi zina apolisi amauza ofalitsa amene awapeza akulalikira kuti akuphwanya malamulo ndipo amawaletsa kulalikira. Ngati mwauzidwa kuchita zimenezi, nthawi yomweyo siyani kulalikirako ndi kuchoka m’gawolo mwaulemu. (Mat. 5:41; Afil. 4:5) Simuyenera kuyesa kuthetsa nkhaniyo panokha mwa kuyamba kukambirana nawo za malamulo amene amatipatsa ufulu wolalikira. Ngati n’kotheka, yesani kukopera nambala ya baji ya wapolisiyo ndiponso nambala ya malo amene iye amayang’anira. Kenako, dziwitsani mwamsanga akulu, ndipo iwo adzadziwitsa ofesi ya nthambi zimene zachitikazo. Mofananamo, ngati woyang’anira nyumba zimene pamakhala anthu ambiri kapena womuimira akuuzani kuti musalalikire nyumba zimenezi, muyenera kuwamvera ndiponso kudziwitsa akulu. Kuchita zinthu mofatsa ndiponso modzichepetsa tikakumana ndi anthu amene ali ndi ulamuliro kungathandize kupewa mavuto ena.—Miy. 15:1; Aroma 12:18.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena