Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 1/15 tsamba 4
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Yofanana
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Zomwe Munganene Pogawira Magazini
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2009
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 1/15 tsamba 4

Zitsanzo za Ulaliki

Nsanja ya Olonda February 1

“Tabwera kuti tikupatseni kapepala aka. Kapepala kameneka kakufotokoza mmene malangizo a m’Baibulo angatithandizire. Kapepala kanu ndi aka. [Apatseni kapepala kakuti, Kodi Baibulo Mumalikhulupirira?] Anthu ena amafuna kudziwa ngati m’Baibulo angapezemo malangizo omwe angawathandize pa ntchito yawo. Taonani zimene lemba ili limanena pa nkhani ya ntchito. [Werengani Mlaliki 3:13.] Magazini iyi ikufotokoza mfundo za m’Baibulo zomwe zingatithandize kuti tizisangalala ndi ntchito yathu.”

Galamukani! February

“Tabwera kuti tikambirane nanu mwachidule nkhani yomwe ili mu Galamukani! ya mwezi uno. Magaziniyi ili ndi yankho la funso ili. [Musonyezeni funso lomwe lili pachikuto cha Galamukani! ya February.] Ndikufuna kumva maganizo anu palemba ili. [Werengani Miyambo 29:11.] Kodi mfundo imeneyi ndi yothandiza masiku ano? [Yembekezerani ayankhe.] Magaziniyi ikutchula mfundo 4 za m’Baibulo ndipo ikufotokoza mmene mfundozi zingatithandizire pa moyo wathu.”

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena