Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 August tsamba 7
  • ‘Kodi Yehova Ndidzamubwezera Chiyani?’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Kodi Yehova Ndidzamubwezera Chiyani?’
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • “Muziyamika pa Chilichonse”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Kodi Mudzachita Zinthu Zosonyeza Kuyamikira Yehova pa Nyengo ya Chikumbutso Ikubwerayi?
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Muzisonyeza Kuyamikira
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Kuyamikira
    Galamukani!—2016
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 August tsamba 7

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MASALIMO 110-118

‘Kodi Yehova Ndidzamubwezera Chiyani?’

Wolemba Masalimo akuimba zeze
Munthu wamangidwa ndi zingwe

Munthu amene analemba Masalimo amenewa ankaona kuti Yehova wamuchitira zazikulu pomupulumutsa ku “zingwe za imfa.” (Sal. 116:3) Iye anatsimikiza mtima kumuthokoza Yehova poyesetsa kuchita zonse zimene Mulunguyo amafuna komanso kukwaniritsa zinthu zonse zimene anamulonjeza.

Kodi ndi zinthu zotani zimene Yehova wandichitira mlungu uno?

Kodi ndingamuthokoze bwanji Yehova chifukwa cha zomwe wandichitira?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena