Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 December tsamba 6
  • Zimene Mulungu Amatiphunzitsa Zimatithandiza Kuti Tisakhale Atsankho

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Mulungu Amatiphunzitsa Zimatithandiza Kuti Tisakhale Atsankho
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Tsankho Likuchitika Padziko Lonse
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Kodi Tsankho Lidzatha Liti?
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Kodi Muli Ndi Mtima Watsankho?
    Galamukani!—2020
  • Mapeto a Tsankho
    Galamukani!—2004
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 December tsamba 6

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Zimene Mulungu Amatiphunzitsa Zimatithandiza Kuti Tisakhale Atsankho

Yehova alibe tsankho. (Mac. 10:34, 35) Iye amalola kuti anthu ochokera “m’dziko lililonse, fuko lililonse, mtundu uliwonse, ndi chinenero chilichonse” akhale atumiki ake. (Chiv. 7:9) Choncho, anthu amene ali mumpingo wachikhristu sayenera kuchita zinthu mwatsankho kapena mokondera. (Yak. 2:1-4) Zimene Mulungu amatiphunzitsa zatithandiza kuti tizisangalala ndi paradaiso wauzimu ndipo timaona anthu akusintha makhalidwe awo. (Yes. 11:6-9) Tikamayesetsa kuchotsa mtima watsankho, timasonyeza kuti tikutsanzira Mulungu.—Aef. 5:1, 2.

Johny ndi Gideon akulandira ana ku Nyumba ya Ufumu

ONERANI VIDIYO YAKUTI, JOHNY NDI GIDEON: ANALI KHOSWE NDI MPHAKA KOMA PANO NDI OGWIRIZANA. KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • N’chifukwa chiyani tinganene kuti zimene Mulungu amatiphunzitsa ndi zimene zingathandize kwambiri pothetsa tsankho kuposa zimene anthu paokha amachita?

  • N’chiyani chimakuchititsani chidwi mukaona mgwirizano umene ulipo pakati pa abale ndi alongo padziko lonse?

  • Kodi Yehova amalemekezedwa bwanji tikamayesetsa kukhalabe ogwirizana monga Akhristu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena