CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | HOSEYA 8-14
Muzipereka Zinthu Zabwino Kwambiri kwa Yehova
Yehova amasangalala ndi nsembe zathu zabwino ndipo amatidalitsa
TIKAKHALA PA UBWENZI NDI YEHOVA
Timapereka kwa Yehova nsembe zathu zomutamanda
Yehova amatikhululukira, amatikonda komanso timakhala naye pa ubwenzi
Timayamikira madalitso amene timapeza chifukwa chomvera malamulo a Yehova ndipo izi zimatithandiza kuti tizifunitsitsa kumutumikirabe
Kodi ndingatani kuti ndizipereka kwa Yehova zinthu zabwino kwambiri?