Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 April tsamba 1
  • Zimene Tinganene

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Tinganene
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • ●○○ ULENDO WOYAMBA
  • ○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA
  • ○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Zimene Tinganene
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 April tsamba 1
Akuchititsa phunziro la Baibulo ku Czech Republic

Akuchititsa phunziro la Baibulo ku Czech Republic

Zimene Tinganene

●○○ ULENDO WOYAMBA

Funso: Kodi mukuganiza kuti tingapeze kuti malangizo omwe angatithandize kuti tizikhala osangalala?

Lemba: Sal. 1:1, 2

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi kukonda ndalama komanso chuma kungatibweretsere mavuto otani?

○●○ ULENDO WOBWEREZA WOYAMBA

Funso: Kodi kukonda ndalama komanso chuma kungatibweretsere mavuto otani?

Lemba: 1 Tim. 6:9, 10

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi kukhala wosangalala kuli ndi ubwino wotani?

○○● ULENDO WOBWEREZA WACHIWIRI

Funso: Kodi kukhala wosangalala kuli ndi ubwino wotani?

Lemba: Miy. 17:22

Funso la Ulendo Wotsatira: Kodi tingatani kuti tizisangalalabe m’banja ngakhale tikukumana ndi mavuto?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena