Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 April tsamba 6
  • Yesu Ali ndi Mphamvu Zoukitsa Anthu Amene Anamwalira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yesu Ali ndi Mphamvu Zoukitsa Anthu Amene Anamwalira
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • “Mlongo Wako Adzauka”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Kodi Kuuka kwa Yesu Kumatithandiza Bwanji?
    Nsanja ya Olonda—2014
  • “Ndili ndi Chiyembekezo mwa Mulungu”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Chiphunzitso cha Kuuka kwa Akufa Chimakukhudzani
    Nsanja ya Olonda—2005
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 April tsamba 6
Yesu akuukitsa mwana wamkazi wa Yairo

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MALIKO 5-6

Yesu Ali ndi Mphamvu Zoukitsa Anthu Amene Anamwalira

5:38-42

  • Mlongo akumva chisoni chifukwa cha imfa ya mwana wake wamkazi ndipo akuyerekezera mwanayo atauka

    Tikamalira chifukwa cha imfa ya munthu amene timam’konda, sizisonyeza kuti sitikhulupirira zoti akufa adzauka (Gen. 23:2)

  • Kuganizira nkhani za m’Baibulo zokhudza anthu amene anaukitsidwa kungatithandize kuti tisamakayikire zoti akufa adzauka

Kodi inuyo mumafuna mutadzaonananso ndi ndani, akufa akamadzaukitsidwa?

Kodi mumamva bwanji mukamaganizira zodzakumananso ndi anthu amenewo?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena