Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 May tsamba 6
  • Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mulungu Amamva Chisoni Tikamavutika?
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
    Pulogalamu ya Msonkhano Wadera ya 2018-2019—Wokhala ndi Woyang’anira Dera
  • ‘Lankhulani Mawu a Mulungu Molimba Mtima’
    Nsanja ya Olonda—2010
  • N’chifukwa Chiyani Mulungu Amalola Kuti Anthufe Tizivutika?
    Nsanja ya Olonda—2014
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 May tsamba 6
Kamtsikana kachiisiraeli kakulankhula ndi mkazi wa Namani

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima

Ngati muli pasukulu, kodi nthawi zina mumachita mantha kulalikira kapena kuwauza anthu ena kuti ndinu wa Mboni za Yehova? Ngati ndi choncho, kodi n’chiyani chingakuthandizeni kuti ‘muzilimba mtima’ kuuza ena za Yehova? (1 Ates. 2:2) Ndipo n’chifukwa chiyani muyenera kuchita zimenezi? Onerani vidiyo yakuti Yehova Akuthandiza Kuti Ukhale Wolimba Mtima, kenako yankhani mafunso otsatirawa:

  1. Sofiya akum’patsa Zowe buku lakuti Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso; ka mnyamata ka mboni kakuwerengera mnzake wakusukulu buku lakuti Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa

    Kodi ndi chitsanzo chiti cha m’Baibulo chomwe chinathandiza Sofiya kukhala wolimba mtima?

  2. Kodi kuyeserera zoti akalankhule kunamuthandiza bwanji Sofiya?

  3. N’chifukwa chiyani muyenera kumalalikira kwa anzanu akusukulu?

  4. Ngati simuli pasukulu, kodi mwaphunzira zotani m’vidiyoyi?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena