Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 October tsamba 3
  • Muzitsanzira Yesu pa Nkhani Yochitira Ena Chifundo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzitsanzira Yesu pa Nkhani Yochitira Ena Chifundo
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • “Anagwidwa ndi Chifundo”
    ‘Bwera Ukhale Wotsatira Wanga’
  • Tizitsanzira Yehova pa Nkhani ya Chifundo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • “Chifundo Chachikulu cha Mulungu Wathu”
    Yandikirani Yehova
  • Sonyezani ‘Chifundo Chachikulu’
    Nsanja ya Olonda—2007
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 October tsamba 3

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOHANE 11-12

Muzitsanzira Yesu pa Nkhani Yochitira Ena Chifundo

Yesu akutonthoza Mariya anthu ena akuona

11:23-26, 33-35, 43, 44

Kodi n’chifukwa chiyani n’zochititsa chidwi kuti Yesu ankachitira kwambiri chifundo anthu ena?

  • Ngakhale kuti sanakumanepo ndi mavuto onse omwe anthu ankakumana nawo, iye ankadziyerekezera kuti ndi munthu winayo n’kumamva ululu umene munthuyo akumva

  • Iye sanachite manyazi kulira pagulu

  • Akaona anthu akuvutika ankachitapo kanthu n’kuwathandiza

Mlongo wachikulire wagwira mlongo wachitsikana ndipo akumutonthoza

Kodi ndingasonyeze bwanji kuti ndimaganizira mmene ena akumvera?

Kodi ndingachite zinthu ziti kuti ndithandize anthu ena?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena