Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 October tsamba 5
  • “Ndakupatsani Chitsanzo”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ndakupatsani Chitsanzo”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Munthu Wamkulu Koposa Onse Achita Utumiki Wodzichepetsa
    Nsanja ya Olonda—1999
  • Yesu Anatipatsa Chitsanzo cha Kudzichepetsa
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Khalani Odzichepetsadi
    Nsanja ya Olonda—2005
  • “Ndine . . . Wodzichepetsa”
    ‘Bwera Ukhale Wotsatira Wanga’
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 October tsamba 5
Yesu akusambitsa mapazi a atumwi ake

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YOHANE 13-14

“Ndakupatsani Chitsanzo”

13:5, 12-15

Pamene Yesu anasambitsa mapazi a ophunzira ake, anawaphunzitsa kuti akhale odzichepetsa komanso azigwira ntchito zooneka zotsika pothandiza abale awo.

Kodi ndingasonyeze bwanji kuti ndine wodzichepetsa . . .

  • Alongo awiri asemphana maganizo

    ndikasemphana maganizo ndi anthu ena?

  • M’bale wina akupereka malangizo kwa mnzake

    ena akandipatsa malangizo?

  • Abale ndi alongo akugwira ntchito yoyeretsa pa Nyumba ya Ufumu

    ndikamagwira nawo ntchito yosamalira kapena kukonza Nyumba ya Ufumu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena