Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsamba 7
  • Muziyesetsa Kumvetsa Nkhani Yonse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muziyesetsa Kumvetsa Nkhani Yonse
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Abale a Yosefe Amuda
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
  • “Tamverani Maloto Amene Ine Ndinalota”
    Nsanja ya Olonda—2014
  • “Kodi Ine Ndatenga Malo a Mulungu?”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Abale Ake a Yosefe Anachita Nsanje Kodi Iwenso Umachita Nsanje?
    Nsanja ya Olonda—2008
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 May tsamba 7
M’bale wachinyamata akuganizira zomwe wawerenga m’Baibulo zokhudza Yosefe. Chithunzi choyamba: Yosefe akuponyedwa m’chitsime chopanda madzi. Chachiwiri: Yosefe akuyenda ndi Amidiyani pa ulendo wopita ku Iguputo. Chachitatu: Potifara akuyankhulana ndi Yosefe ndipo mkazi wa Potifara akuwayang’ana ali chapatali.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Muziyesetsa Kumvetsa Nkhani Yonse

Mukamawerenga nkhani za m’Baibulo, muziyesetsa kumvetsa nkhani yonse. Dziwani mmene zinthu zinalili pa nthawi yomwe nkhaniyo inkachitika, anthu otchulidwa mu nkhaniyo, komanso zimene zinawachititsa kuchita zomwe anachitazo. M’maganizo mwanu, onani malo omwe kunkachitikira nkhaniyo, phokoso lomwe linkamveka, fungo lomwe linkamveka, komanso mmene anthu a m’nkhaniyo ankamvera.

ONERANI MBALI INA YA VIDIYO YAKUTI MUZIYESETSA KUMVETSA ZIMENE MUMAWERENGA M’BAIBULO NDIPO KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Yosefe asanagulitsidwe kukhala kapolo.

    Kodi ndi zinthu ziti zomwe zinachititsa kuti pakhale kusamvana pakati pa Yosefe ndi azichimwene ake?

  • Yosefe akuyenda ndi Amidiyani pa ulendo wopita ku Iguputo.

    Kodi ndi zinthu ziti zimene zinkachititsa kuti azichimwene ake a Yosefe azichita zinthu mosaganiza bwino nthawi zina?

  • Zimene Yakobo anachita kuti athetse kusamvana ndi Esau. Chithunzi choyamba: Yakobo akupemphera. Chachiwiri: Yakobo akuweramira Esau. Chachitatu: Esau akukumbatira Yakobo.

    Kodi Malemba amatiuza zotani zokhudza Yakobo, bambo ake a Yosefe?

  • Kodi Yakobo anapereka chitsanzo chotani kwa ana ake pa nkhani yothetsa kusamvana?

  • Kodi vidiyoyi yakuthandizani bwanji?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena