-
Genesis 36:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 Potsiriza, ana a Oholibama mkazi wa Esau ndi awa: Mfumu Yeusi, Mfumu Yalamu ndi Mfumu Kora. Amenewa ndi amene anali mafumu akubanja la Oholibama mkazi wa Esau, amenenso anali mwana wa Ana.
-