Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 12:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Koma ngati banja lili lalingʼono moti silingamalize kudya nkhosa yonseyo, banjalo lidzaitane banja lina loyandikana nalo kuti adzadyere limodzi mʼnyumba mwawo, mogwirizana ndi chiwerengero cha anthu. Muziganizira mmene munthu aliyense amadyera kuti mudziwe kuchuluka kwa nyama imene ikufunika.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena