-
Ekisodo 13:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Farao atakana mouma mtima kuti tichoke,+ Yehova anapha mwana woyamba kubadwa aliyense mʼdziko la Iguputo, kuyambira mwana woyamba kubadwa wa munthu mpaka mwana woyamba kubadwa wa nyama.+ Nʼchifukwa chake tikupereka nsembe kwa Yehova ana onse a nyama oyamba kubadwa* ndiponso tikuwombola mwana wathu wamwamuna aliyense woyamba kubadwa.’
-