-
Ekisodo 30:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
8 Komanso Aroni akamayatsa nyalezo madzulo, aziwotcha zofukizazo. Zimenezi ndi zofukiza zoyenera kuperekedwa kwa Yehova nthawi zonse mʼmibadwo yanu yonse.
-