Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 11:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndiyeno panali amuna awiri amene anatsalira mumsasa. Mayina awo anali Eledadi ndi Medadi. Amenewanso analandira mzimuwo chifukwa anali mʼgulu la anthu amene analembedwa mayina, koma sanapite nawo kuchihema. Choncho iwonso anayamba kuchita zinthu ngati aneneri mumsasamo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena