-
Numeri 19:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 Munthu woteroyo azidziyeretsa ndi madzi oyeretsera aja pa tsiku lachitatu, ndipo pa tsiku la 7 azikhala woyera. Koma akapanda kudziyeretsa pa tsiku lachitatu, sadzakhala woyera pa tsiku la 7.
-