-
Numeri 29:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 Muzipereka nsembe zimenezi kuwonjezera pa nsembe yopsereza ya mwezi ndi mwezi, limodzi ndi nsembe yake yambewu.+ Muzizipereka kuwonjezeranso pa nsembe yopsereza ya tsiku ndi tsiku, limodzi ndi nsembe yake yambewu,+ limodzinso ndi nsembe zachakumwa.+ Muzipereka nsembe zopserezazo mogwirizana ndi dongosolo lake la nthawi zonse, monga nsembe zowotcha pamoto zakafungo kosangalatsa* kwa Yehova.
-