-
Yoswa 18:20Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
20 Kumʼmawa, malire ake anali mtsinje wa Yorodano. Ichi chinali cholowa cha ana a Benjamini motsatira mabanja awo, ndi malire ake kuzungulira gawo lonse.
-